Masalimo 35:2 - Buku Lopatulika2 Gwirani chikopa chotchinjiriza, ukani kundithandiza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Gwirani chikopa chotchinjiriza, ukani kundithandiza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Gwirani chishango ndi lihawo, ndipo fulumirani mundithandize. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Tengani chishango ndi lihawo; dzukani ndipo bwerani mundithandize. Onani mutuwo |