Masalimo 34:22 - Buku Lopatulika22 Yehova aombola moyo wa anyamata ake, ndipo sadzawatsutsa kumlandu onse akukhulupirira Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Yehova aombola moyo wa anyamata ake, ndipo sadzawatsutsa kumlandu onse akukhulupirira Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Chauta amaombola moyo wa atumiki ake. Palibe wothaŵira kwa Iye amene adzalangidwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Yehova amawombola atumiki ake; aliyense amene amathawira kwa Iye sadzapezeka wolakwa. Onani mutuwo |