Masalimo 34:21 - Buku Lopatulika21 Mphulupulu idzamupha woipa; ndipo adzawatsutsa kumlandu iwo akudana naye wolungama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Mphulupulu idzamupha woipa; ndipo adzawatsutsa kumlandu iwo akudana naye wolungama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Choipa chitsata mwini, anthu odana ndi munthu wa Mulungu adzalangidwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Choyipa chidzapha anthu oyipa; adani a olungama adzapezeka olakwa. Onani mutuwo |