Masalimo 34:18 - Buku Lopatulika18 Yehova ali pafupi ndi iwo a mtima wosweka, apulumutsa iwo a mzimu wolapadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Yehova ali pafupi ndi iwo a mtima wosweka, apulumutsa iwo a mzimu wolapadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Chauta amakhala pafupi ndi anthu a mtima wosweka, amapulumutsa otaya mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Yehova ali pafupi kwa osweka mtima ndipo amapulumutsa iwo amene asweka mu mzimu. Onani mutuwo |