Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 34:17 - Buku Lopatulika

17 Iwowo anaitana, ndipo Yehova anawamva, nawalanditsa kumasautso ao onse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Iwowo anaitana, ndipo Yehova anawamva, nawalanditsa kumasautso ao onse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Pamene anthu ake akulira kuti aŵathandize, Chauta amamva naŵapulumutsa m'mavuto ao onse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Olungama amafuwula, ndipo Yehova amawamva; Iye amawalanditsa ku mavuto awo onse.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 34:17
17 Mawu Ofanana  

Masiku omwe aja Hezekiya anadwala pafupi imfa; ndipo anapemphera kwa Yehova; ndi Iye ananena naye, nampatsa chizindikiro chodabwitsa.


Taona, Mulungu sakana munthu wangwiro; kapena kugwiriziza ochita zoipa.


Zikhale pamaso pa Yehova chikhalire, kuti adule chikumbukiro chao kuchichotsera kudziko lapansi.


Maso a Yehova ali pa olungama mtima, ndipo makutu ake atchereza kulira kwao.


Masautso a wolungama mtima achuluka, koma Yehova amlanditsa mwa onsewa.


Munthu uyu wozunzika anafuula, ndipo Yehova anamumva, nampulumutsa m'masautso ake onse.


Koma ine, mwa kuchuluka kwa chifundo chanu ndidzalowa m'nyumba yanu; ndidzagwada kuyang'ana Kachisi wanu woyera ndi kuopa Inu.


Adaniwo atha psiti, apululuka nthawi zonse; ndipo mizindayo mwaipasula, chikumbukiro chao pamodzi chatha.


Adzandifuulira Ine ndipo ndidzamyankha; kunsautso ndidzakhala naye pamodzi; ndidzamlanditsa, ndi kumchitira ulemu.


Amayesa wolungama wodala pomkumbukira; koma dzina la oipa lidzavunda.


Ndipo padzakhala kuti iwo asanaitane Ine, ndidzayankha; ndipo ali chilankhulire, Ine ndidzamva.


ndipo ndidzaikira munthu uyu nkhope yanga imtsutse, ndi kumuyesa chodabwitsa, ndi chizindikiro, ndi mwambi, ndi kumsadza pakati pa anthu anga; ndipo mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.


Angakhale alowa ndende pamaso pa adani ao, kumeneko ndidzalamulira lupanga, ndipo lidzawapha; ndipo ndidzayang'anitsa maso anga kwa iwowa, kuwachitira choipa, si chokoma ai.


Ndinati, Ndikadawauzira ndithu, ndikadafafaniza chikumbukiro chao mwa anthu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa