Masalimo 34:17 - Buku Lopatulika17 Iwowo anaitana, ndipo Yehova anawamva, nawalanditsa kumasautso ao onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Iwowo anaitana, ndipo Yehova anawamva, nawalanditsa kumasautso ao onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Pamene anthu ake akulira kuti aŵathandize, Chauta amamva naŵapulumutsa m'mavuto ao onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Olungama amafuwula, ndipo Yehova amawamva; Iye amawalanditsa ku mavuto awo onse. Onani mutuwo |