Masalimo 34:16 - Buku Lopatulika16 Nkhope ya Yehova itsutsana nao akuchita zoipa, kudula chikumbukiro chao padziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Nkhope ya Yehova itsutsana nao akuchita zoipa, kudula chikumbukiro chao pa dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Koma Chauta amaŵakwiyira anthu ochita zoipa, anthuwo sadzakumbukikanso pansi pano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 nkhope ya Yehova ikutsutsana ndi amene amachita zoyipa, kuwachotsa kuti asawakumbukirenso pa dziko lapansi. Onani mutuwo |