Masalimo 34:15 - Buku Lopatulika15 Maso a Yehova ali pa olungama mtima, ndipo makutu ake atchereza kulira kwao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Maso a Yehova ali pa olungama mtima, ndipo makutu ake atchereza kulira kwao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Ngati mumvera Chauta, adzakuyang'anirani ndipo adzayankha kupempha kwanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Maso a Yehova ali pa olungama ndipo makutu ake ali tcheru kumva kulira kwawo; Onani mutuwo |