Masalimo 33:22 - Buku Lopatulika22 Yehova, chifundo chanu chikhale pa ife, monga takuyembekezani Inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Yehova, chifundo chanu chikhale pa ife, monga takuyembekezani Inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Inu Chauta, chikondi chanu chosasinthika chikhale pa ife, chifukwa timakhulupirira Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Chikondi chanu chosatha chikhale pa ife Inu Yehova, pamene tikuyembekeza kwa Inu. Onani mutuwo |