Masalimo 33:21 - Buku Lopatulika21 Pakuti mtima wathu udzakondwera mwa Iye, chifukwa takhulupirira dzina lake loyera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Pakuti mtima wathu udzakondwera mwa Iye, chifukwa takhulupirira dzina lake loyera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Mitima yathu imasangalala mwa Chauta, popeza kuti timadalira dzina lake loyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Mwa Iye mitima yathu imakondwera, pakuti ife timadalira dzina lake loyera. Onani mutuwo |