Masalimo 33:18 - Buku Lopatulika18 Taonani, diso la Yehova lili pa iwo akumuopa Iye, pa iwo akuyembekeza chifundo chake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Taonani, diso la Yehova lili pa iwo akumuopa Iye, pa iwo akuyembekeza chifundo chake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Chauta amayang'ana anthu omumvera, ndi odalira chikondi chake chosasinthika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Koma maso a Yehova ali pa iwo amene amaopa Iye; amene chiyembekezo chawo chili mʼchikondi chake chosatha, Onani mutuwo |