Masalimo 33:16 - Buku Lopatulika16 Palibe mfumu yoti gulu lalikulu limpulumutsa, mphamvu yaikulu siichilanditsa chiphona. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Palibe mfumu yoti gulu lalikulu limpulumutsa, mphamvu yaikulu siichilanditsa chiphona. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Mfumu siipulumuka chifukwa cha kukula kwa gulu lake la ankhondo. Wankhondo sapulumuka chifukwa chakuti ali ndi mphamvu zambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Palibe mfumu imene imapulumutsidwa chifukwa cha kukula kwa gulu lake lankhondo; palibe msilikali amene amathawa ndi mphamvu zake zazikulu. Onani mutuwo |