Masalimo 33:13 - Buku Lopatulika13 Yehova apenyerera m'mwamba; aona ana onse a anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Yehova apenyerera m'mwamba; aona ana onse a anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Chauta ali kumwamba, amayang'ana pansi ndi kuwona anthu onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Kuchokera kumwamba Yehova amayangʼana pansi ndi kuona anthu onse; Onani mutuwo |