Masalimo 31:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo simunandipereke m'dzanja la mdani; munapondetsa mapazi anga pali malo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo simunandipereka m'dzanja la mdani; munapondetsa mapazi anga pali malo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Simudandipereke m'manja mwa adani anga, koma mwandiika pa malo otambalala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Inu simunandipereke kwa mdani koma mwayika mapazi anga pa malo otakasuka. Onani mutuwo |