Masalimo 31:18 - Buku Lopatulika18 Ikhale yosalankhula milomo ya mabodza, imene imalankhula mwachipongwe pa olungama mtima, ndi kudzikuza ndi kunyoza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ikhale yosalankhula milomo ya mabodza, imene imalankhula mwachipongwe pa olungama mtima, ndi kudzikuza ndi kunyoza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Onse onyada ndi onama olankhula mwamwano ndi monyoza kwa anthu abwino, muŵakhalitse chete. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Milomo yawo yabodzayo ikhale chete, pakuti chifukwa cha kunyada ayankhula modzikuza kutsutsana ndi wolungama. Onani mutuwo |