Masalimo 31:12 - Buku Lopatulika12 Ndaiwalika m'mtima monga wakufa, ndikhala monga chotengera chosweka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndaiwalika m'mtima monga wakufa, ndikhala monga chotengera chosweka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Andiiŵala kotheratu ngati munthu wakufa. Ndasanduka ngati chiŵiya chosweka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ine ndinayiwalika kwa iwo ngati kuti ndinamwalira; ndakhala ngati mʼphika wosweka. Onani mutuwo |