Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 29:7 - Buku Lopatulika

7 Liu la Yehova ligawa malawi a moto.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Liu la Yehova ligawa malawi a moto.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Liwu la Chauta likutulutsa malaŵi amoto.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Liwu la Yehova limakantha ngati kungʼanima kwa mphenzi.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 29:7
9 Mawu Ofanana  

Akumveketsa pansi pa thambo ponse, nang'anipitsa mphezi yake ku malekezero a dziko lapansi.


Kodi ukhoza kutumiza mphezi kuti zimuke, ndi kunena nawe, Tili pano?


Ndipo anatuma mivi yake nawabalalitsa; inde mphezi zaunyinji, nawamwaza.


Liu la bingu lanu linatengezanatengezana; mphezi zinaunikira ponse pali anthu; dziko lapansi linanjenjemera ndi kugwedezeka.


Pamenepo Mose anasamulira ndodo yake kuthambo, ndipo Yehova anatumiza bingu ndi matalala, ndi moto unatsikira pansi; ndipo Yehova anavumbitsa matalala padziko la Ejipito.


Ndipo panatuluka moto pamaso pa Yehova, nuwatha, nafa iwo pamaso ya Yehova.


Ndipo moto unatuluka kwa Yehova, ndi kunyeketsa amuna mazana awiri ndi makumi asanu aja akubwera nacho chofukiza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa