Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 29:6 - Buku Lopatulika

6 Aitumphitsa monga mwanawang'ombe; Lebanoni ndi Sirioni monga msona wa njati.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Aitumphitsa monga mwanawang'ombe; Lebanoni ndi Sirioni monga msona wa njati.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Amagwedeza phiri la Lebanoni kuti lizivinavina ngati likonyani, amavinitsa phiri la Sirioni ngati mwanawanjati.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Iye amachititsa Lebanoni kulumphalumpha ngati mwana wangʼombe, Siriyoni ngati mwana wa njati:

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 29:6
7 Mawu Ofanana  

Koma munakweza nyanga yanga ngati ya njati; anandidzoza mafuta atsopano.


Mulungu awatulutsa mu Ejipito; mphamvu yake ikunga ya njati.


(Asidoni alitcha Heremoni Sirioni, koma Aamori alitcha Seniri);


Ndipo ndinaona, mpando wachifumu waukulu woyera, ndi Iye wakukhalapo, amene dziko ndi m'mwamba zinathawa pamaso pake, ndipo sanapezedwe malo ao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa