Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 25:22 - Buku Lopatulika

22 Ombolani Israele, Mulungu, m'masautso ake onse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Ombolani Israele, Mulungu, m'masautso ake onse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Inu Mulungu apulumutseni m'mavuto ao onse anthu anu Aisraele.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Wombolani Israeli Inu Mulungu, ku mavuto ake onse!

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 25:22
5 Mawu Ofanana  

Mupempherere mtendere wa Yerusalemu; akukonda inu adzaona phindu.


Ndipo adzaombola Israele ku mphulupulu zake zonse.


Mwenzi chipulumutso cha Israele chitachokera ku Ziyoni! Pakubweretsa Yehova anthu ake a m'nsinga, pamenepo adzakondwera Yakobo, nadzasekera Israele.


M'mazunzo ao onse Iye anazunzidwa, ndipo mthenga wakuimirira pamaso pake anawapulumutsa; m'kukonda kwake ndi m'chisoni chake Iye anawaombola, nawabereka nawanyamula masiku onse akale.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa