Masalimo 25:21 - Buku Lopatulika21 Ungwiro ndi kuongoka mtima zindisunge, pakuti ndayembekezera Inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ungwiro ndi kuongoka mtima zindisunge, pakuti ndayembekezera Inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Kukhulupirika kwanga ndi kulungama kwanga kunditeteze, popeza kuti ndakukhulupirirani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Kukhulupirika ndi kulungama kwanga kunditeteze, chifukwa chiyembekezo changa chili mwa Inu. Onani mutuwo |