Masalimo 25:18 - Buku Lopatulika18 Penyani mazunzo anga ndi zovuta zanga; ndipo khululukirani zolakwa zanga zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Penyani mazunzo anga ndi zovuta zanga; ndipo khululukirani zolakwa zanga zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Penyani mazunzo anga ndi mavuto anga, ndipo mundikhululukire machimo anga onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Penyani mazunzo anga ndi zovuta zanga ndipo mufafanize machimo anga onse. Onani mutuwo |