Masalimo 25:13 - Buku Lopatulika13 Moyo wake udzakhala mokoma; ndi mbumba zake zidzalandira dziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Moyo wake udzakhala mokoma; ndi mbumba zake zidzalandira dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Munthu ameneyo adzakhaladi pabwino, ana ake adzalandira dziko kuti likhale choloŵa chao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Iye adzakhala pa ulemerero masiku ake onse, ndipo zidzukulu zake zidzalandira dziko ngati cholowa chawo. Onani mutuwo |