Masalimo 25:12 - Buku Lopatulika12 Munthuyo wakuopa Yehova ndani? Adzamlangiza iye njira adzasankheyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Munthuyo wakuopa Yehova ndani? Adzamlangiza iye njira adzasankheyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Kodi pali munthu woopa Chauta? Munthuyo Chauta adzamphunzitsa njira yoti aitsate. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Tsono ndani munthu amene amaopa Yehova? Yehova adzamulangiza njira yoti ayitsate. Onani mutuwo |