Masalimo 25:11 - Buku Lopatulika11 Chifukwa cha dzina lanu, Yehova, ndikhululukireni kusakaza kwanga, pakuti ndiko kwakukulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Chifukwa cha dzina lanu, Yehova, ndikhululukireni kusakaza kwanga, pakuti ndiko kwakukulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Malinga ndi ulemerero wa dzina lanu, Inu Chauta, mundikhululukire machimo anga pakuti mlandu wanga ndi waukulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Chifukwa cha dzina lanu, Inu Yehova, khululukireni mphulupulu zanga, ngakhale kuti ndi zochuluka. Onani mutuwo |