Masalimo 22:31 - Buku Lopatulika31 Iwo adzadza nadzafotokozera chilungamo chake kwa anthu akadzabadwa, kuti Iye anachichita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Iwo adzadza nadzafotokozera chilungamo chake kwa anthu akadzabadwa, kuti Iye anachichita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Adzalalika za chipulumutso chake kwa anthu amene mpaka tsopano sanabadwe, ponena kuti Chauta ndiye adapulumutsa anthu ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Iwo adzalengeza za chilungamo chake kwa anthu amene pano sanabadwe pakuti Iye wachita zimenezi. Onani mutuwo |