Masalimo 18:49 - Buku Lopatulika49 Chifukwa chake Yehova ndidzakuyamikani mwa amitundu, ndipo dzina lanu ndidzaliimbira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201449 Chifukwa chake Yehova ndidzakuyamikani mwa amitundu, ndipo dzina lanu ndidzaliimbira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa49 Chifukwa cha zimenezi ndidzakutamandani Inu Chauta, pakati pa mitundu ya anthu, ndidzaimba nyimbo zotamanda dzina lanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero49 Choncho ine ndidzakutamandani pakati pa anthu a mitundu ina, Inu Yehova; ndidzayimba nyimbo zotamanda dzina lanu. Onani mutuwo |