Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 18:48 - Buku Lopatulika

48 Andipulumutsa kwa adani anga. Inde mundikweza pa iwo akundiukira ine, mundikwatula kwa munthu wachiwawa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

48 Andipulumutsa kwa adani anga. Inde mundikweza pa iwo akundiukira ine, mundikwatula kwa munthu wachiwawa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

48 Ndiye amene adandipulumutsa kwa adani anga. Zoonadi Inu mudandikweza pamwamba pa ondiwukira, mudandilanditsa kwa anthu ankhanza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

48 amene amandipulumutsa mʼmanja mwa adani anga. Inu munandikuza kuposa adani anga; munandilanditsa mʼmanja mwa anthu ankhanza.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 18:48
9 Mawu Ofanana  

Ndilanditseni, Yehova, kwa munthu woipa; ndisungeni kwa munthu wachiwawa;


Munthu wamlomo sadzakhazikika padziko lapansi; choipa chidzamsaka munthu wachiwawa kuti chimgwetse.


Ndilindireni Yehova, ndisalowe m'manja mwa woipa; ndisungeni kwa munthu wachiwawa; kwa iwo akuti akankhe mapazi anga.


Chovuta chake chidzambwerera mwini, ndi chiwawa chake chidzamgwera pakati pamutu pake.


Mulungu, odzikuza andiukira, ndi msonkhano wa anthu oopsa afuna moyo wanga, ndipo sanaike Inu pamaso pao.


Muli nao mkono wanu wolimba; m'dzanja mwanu muli mphamvu, dzanja lamanja lanu nlokwezeka.


Mwa ichinso Mulungu anamkwezetsa Iye, nampatsa dzina limene liposa maina onse,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa