Masalimo 18:46 - Buku Lopatulika46 Yehova ngwa moyo; ndipo lidalitsike thanthwe langa; nakwezeke Mulungu wa chipulumutso changa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201446 Yehova ngwa moyo; ndipo lidalitsike thanthwe langa; nakwezeke Mulungu wa chipulumutso changa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa46 Chauta ndi wamoyo. Litamandike thanthwe langa, alemekezeke Mulungu wondipulumutsa, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero46 Yehova ndi wamoyo! Litamandidwe Thanthwe langa! Akuzike Mulungu Mpulumutsi wanga! Onani mutuwo |