Masalimo 18:45 - Buku Lopatulika45 Alendo adzafota, nadzatuluka monjenjemera m'ngaka mwao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201445 Alendo adzafota, nadzatuluka monjenjemera m'ngaka mwao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa45 Anthu a mitundu ina adataya mtima, adatuluka m'malinga mwao ali njenjenje. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero45 Iwo onse anataya mtima; anatuluka mʼmalinga awo akunjenjemera. Onani mutuwo |