Masalimo 18:38 - Buku Lopatulika38 Ndidzawapyoza kuti sangakhoze kuuka, adzagwa pansi pa mapazi anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Ndidzawapyoza kuti sangakhoze kuuka, adzagwa pansi pa mapazi anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Ndimaŵakantha koopsa kotero kuti sangathenso kudzuka, ndidaŵapondereza ndi mapazi anga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Ndinakantha adaniwo kotero kuti sanathenso kudzuka; anagwera pa mapazi anga. Onani mutuwo |