Masalimo 18:36 - Buku Lopatulika36 Mwandipondetsa patalipatali, sanaterereke mapazi anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Mwandipondetsa patalipatali, sanaterereka mapazi anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Mudandikuzira njira yanga kuti ndiyendemo bwino, choncho mapazi anga sadaterereke. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Munakulitsa njira yoyendamo ine, kuti mapazi anga asaguluke. Onani mutuwo |