Masalimo 18:34 - Buku Lopatulika34 Aphunzitsa manja anga agwire nkhondo; kuti walifuka uta wamkuwa ndi manja anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Aphunzitsa manja anga agwire nkhondo; kuti walifuka uta wamkuwa ndi manja anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Amaphunzitsa manja anga kamenyedwe ka nkhondo, kotero kuti ndingathe kupinda uta wachitsulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Iye amaphunzitsa manja anga kuchita nkhondo; manja anga amatha kuthyola uta wachitsulo. Onani mutuwo |