Masalimo 18:28 - Buku Lopatulika28 Pakuti Inu muyatsa nyali yanga; Yehova, Mulungu wanga, aunikira mdima wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Pakuti Inu muyatsa nyali yanga; Yehova, Mulungu wanga, aunikira mdima wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Ndithu, Inu mumayatsa nyale ya moyo wanga. Chauta, Mulungu wanga, amandiwunikira mu mdima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Inu Yehova, sungani nyale yanga kuti iziyakabe; Mulungu wanga wasandutsa mdima wanga kukhala kuwunika. Onani mutuwo |