Masalimo 18:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo ndinakhala wangwiro ndi Iye, ndipo ndinadzisunga wosachita choipa changa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo ndinakhala wangwiro ndi Iye, ndipo ndinadzisunga wosachita choipa changa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Ndinalibe mlandu pamaso pake, ndinkalewa zoipa m'moyo mwanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Ndakhala moyo wosalakwa pamaso pake ndipo ndakhala ndi kupewa tchimo. Onani mutuwo |