Masalimo 150:5 - Buku Lopatulika5 Mlemekezeni ndi nsanje zomveka: Mlemekezeni ndi nsanje zoliritsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mlemekezeni ndi nsanje zomveka: Mlemekezeni ndi nsanje zoliritsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mtamandeni ndi ziwaya zamalipenga zolira, mtamandeni ndi ziwaya zamalipenga zolira kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mutamandeni ndi ziwaya zolira za malipenga, mutamandeni ndi ziwaya zolira kwambiri. Onani mutuwo |
Ndipo kunali, pakuchita limodzi amalipenga ndi oimba, kumveketsa mau amodzi akulemekeza ndi kuyamika Yehova, ndi pakukweza mau ao pamodzi ndi malipenga, ndi nsanje, ndi zoimbira zina, ndi kulemekeza Yehova, ndi kuti, Pakuti Iye ndiye wabwino, pakuti chifundo chake chikhala chikhalire; pamenepo mtambo unadzaza nyumbayi, ndiyo nyumba ya Yehova;