Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 147:7 - Buku Lopatulika

7 Yamikani Yehova ndi kuthira mang'ombe; muimbireni Mulungu wathu zomlemekeza pazeze:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Yamikani Yehova ndi kuthira mang'ombe; muimbireni Mulungu wathu zomlemekeza pazeze:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Imbirani Chauta mothokoza, imbirani Mulungu wathu nyimbo yokoma ndi pangwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Imbirani Yehova ndi mayamiko; imbani nyimbo kwa Mulungu ndi pangwe.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 147:7
8 Mawu Ofanana  

Imbirani Mulungu, maufumu a dziko lapansi inu; imbirani Ambuye zomlemekeza.


Muimbireni Yehova zomlemekeza ndi zeze; ndi zeze ndi mau a salimo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa