Masalimo 147:19 - Buku Lopatulika19 Aonetsa mau ake kwa Yakobo; malemba ake, ndi maweruzo ake kwa Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Aonetsa mau ake kwa Yakobo; malemba ake, ndi maweruzo ake kwa Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Amadziŵitsa Yakobe mau ake, amaphunzitsa Israele malamulo ake ndi malangizo ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Iye anawulula mawu ake kwa Yakobo, malamulo ake ndi zophunzitsa zake kwa Israeli. Onani mutuwo |