Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 147:16 - Buku Lopatulika

16 Apatsa chipale chofewa ngati ubweya; awaza chisanu ngati phulusa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Apatsa chipale chofewa ngati ubweya; awaza chisanu ngati phulusa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Amagwetsa chisanu chambee ngati ubweya. Amamwaza chipale ngati phulusa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Amagwetsa chisanu ngati ubweya ndi kumwaza chipale ngati phulusa.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 147:16
6 Mawu Ofanana  

Pakuti anena kwa chipale chofewa, Ugwe padziko, momwemonso kwa mvula, ndi kwa mvumbi waukulu.


Kodi unalowa m'zosungiramo chipale chofewa? Kapena unapenya zosungiramo matalala,


Chipale chinatuluka m'mimba ya yani? Ndi chisanu chochokera m'mwamba anachibala ndani?


moto ndi matalala, chipale chofewa ndi nkhungu; mphepo ya namondwe, yakuchita mau ake;


Pakuti monga mvula imagwa pansi ndi matalala, kuchokera kumwamba yosabwerera komweko, koma ikhamiza nthaka ndi kuibalitsa, ndi kuiphukitsa, ndi kuipatsitsa mbeu kwa wobzala, ndi chakudya kwa wakudya;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa