Masalimo 147:14 - Buku Lopatulika14 Ndiye amene akhalitsa malire anu mumtendere; akukhutitsani ndi tirigu wakucha bwino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndiye amene akhalitsa malire anu mumtendere; akukhutitsani ndi tirigu wakucha bwino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Amadzetsa mtendere m'malire a dziko lako, amakudyetsa pokupatsa ufa wa tirigu wosalala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Iye amabweretsa mtendere mʼmalire mwako ndi kukukhutitsa ndi ufa wa tirigu wosalala. Onani mutuwo |