Masalimo 147:11 - Buku Lopatulika11 Yehova akondwera nao akumuopa Iye, iwo akuyembekeza chifundo chake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Yehova akondwera nao akumuopa Iye, iwo akuyembekeza chifundo chake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Koma Chauta amakondwera ndi anthu omuwopa, amene amadalira chikondi chake chosasinthika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Yehova amakondwera ndi amene amamuopa, amene chiyembekezo chawo chili mʼchikondi chake chosasinthika. Onani mutuwo |