Masalimo 145:18 - Buku Lopatulika18 Yehova ali pafupi ndi onse akuitanira kwa Iye, onse akuitanira kwa Iye m'choonadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Yehova ali pafupi ndi onse akuitanira kwa Iye, onse akuitanira kwa Iye m'choonadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Chauta ali pafupi ndi onse amene amamutama mopemba. Ali pafupi ndi onse amene amamutama mokhulupirika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Yehova ali pafupi ndi onse amene amamuyitana, onse amene amamuyitana Iye mʼchoonadi. Onani mutuwo |