Masalimo 145:12 - Buku Lopatulika12 Kudziwitsa ana a anthu zamphamvu zake, ndi ulemerero waukulu wa ufumu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Kudziwitsa ana a anthu zamphamvu zake, ndi ulemerero waukulu wa ufumu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 kuti adziŵitse anthu onse za ntchito zanu zamphamvu, kutinso asimbe za ulemerero ndi za ufumu wanu waukulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 kuti anthu onse adziwe za machitidwe anu amphamvu ndi ulemerero wokongola wa ufumu wanu. Onani mutuwo |