Masalimo 145:11 - Buku Lopatulika11 Adzanenera ulemerero wa ufumu wanu, adzalankhulira mphamvu yanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Adzanenera ulemerero wa ufumu wanu, adzalankhulira mphamvu yanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Adzalankhula za ulemerero wa ufumu wanu, adzasimba za mphamvu zanu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Iwo adzafotokoza za ulemerero wa ufumu wanu ndi kuyankhula za mphamvu yanu, Onani mutuwo |