Masalimo 144:6 - Buku Lopatulika6 Ng'animitsani mphezi, ndi kuwabalalitsa; tumizani mivi yanu, ndi kuwapirikitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ng'animitsani mphezi, ndi kuwabalalitsa; tumizani mivi yanu, ndi kuwapirikitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ng'animitsani zing'aning'ani ndi kuŵamwaza adani anga. Ponyani mivi yanu, ndi kuŵapirikitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Tumizani zingʼaningʼani ndi kubalalitsa adani; ponyani mivi yanu ndi kuwathamangitsa. Onani mutuwo |