Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 144:5 - Buku Lopatulika

5 Weramutsani thambo lanu, Yehova, nimutsike: Khudzani mapiri ndipo adzafuka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Weramutsani thambo lanu, Yehova, nimutsike: Khudzani mapiri ndipo adzafuka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Ng'ambani thambo, Inu Chauta, ndi kutsikira pansi. Khudzani mapiri kuti afuke nthunzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Ngʼambani mayiko akumwamba, Inu Yehova, ndipo tsikani pansi; khudzani mapiri kuti atulutse utsi.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 144:5
8 Mawu Ofanana  

amene apenyerera padziko lapansi, ndipo linjenjemera; akhudza mapiri, ndipo afuka.


Ndipo anaberekeka pa kerubi, nauluka; nauluka msanga pa mapiko a mphepo.


Ndipo Iye anaweramitsa thambo, natsika; ndipo pansi pa mapazi ake panali mdima bii.


Ndipo phiri la Sinai linafuka monsemo, popeza Yehova anatsikira m'moto pamenepo; ndi utsi wake unakwera ngati utsi wa m'ng'anjo, ndi phiri lonse linagwedezeka kwambiri.


Pakuti simunayandikire phiri lokhudzika, ndi lakupsa moto, ndi pakuda bii, ndi mdima, ndi namondwe,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa