Masalimo 144:13 - Buku Lopatulika13 Kuti nkhokwe zathu zidzale, kutipatsa za mitundumitundu; ndi kuti nkhosa zathu ziswane zikwizikwi, inde zikwi khumi kubusako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Kuti nkhokwe zathu zidzale, kutipatsa za mitundumitundu; ndi kuti nkhosa zathu ziswane zikwizikwi, inde zikwi khumi kubusako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Nkhokwe zathu zikhale zodzaza, zisunge zokolola za mtundu uliwonse. Nkhosa zathu zibale ana zikwizikwi m'mabusa athu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Nkhokwe zathu zidzakhala zodzaza ndi zokolola za mtundu uliwonse. Nkhosa zathu zidzaswana miyandamiyanda pa mabusa athu. Onani mutuwo |