Masalimo 144:12 - Buku Lopatulika12 Kuti ana athu aamuna akhale ngati mmera udakula usanakhwime; ana athu aakazi ngati nsanamira za kungodya, zosema zikometsere nyumba ya mfumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Kuti ana athu amuna akhale ngati mmera udakula usanakhwime; ana athu akazi ngati nsanamira za kungodya, zosema zikometsere nyumba ya mfumu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ana athu aamuna pachinyamata pao akhale amphamvu ngati mitengo, ana athu aakazi akhale okongola ngati nsanamira zozokotedwa zapangodya, zoti zikometse nyumba yaufumu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ndipo ana aamuna pa chinyamata chawo adzakhala ngati mbewu yosamalidwa bwino, ana athu aakazi adzakhala ngati zipilala zosemedwa bwino, zokongoletsera nyumba yaufumu. Onani mutuwo |