Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 144:11 - Buku Lopatulika

11 Ndilanditseni ndi kundipulumutsa kudzanja la alendo, amene pakamwa pao alankhula zachabe, ndi dzanja lao lamanja ndilo dzanja lachinyengo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndilanditseni ndi kundipulumutsa kudzanja la alendo, amene pakamwa pao alankhula zachabe, ndi dzanja lao lamanja ndilo dzanja lachinyengo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Landitseni kwa adani ankhalwe, mundipulumutse m'manja mwa akunja, amene amalankhula zabodza, ndipo amalumbira zonama.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Landitseni ndi kundipulumutsa, mʼmanja mwa anthu achilendo, amene pakamwa pawo ndi podzaza ndi mabodza, amene dzanja lawo lamanja ndi lachinyengo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 144:11
6 Mawu Ofanana  

Amanena za bodza munthu yense ndi mnansi wake, amanena ndi mlomo wothyasika, ndi mitima iwiri.


Iye adya phulusa; mtima wodzinyenga wampambutsa, kuti iye sangapulumutse moyo wake, pena kunena, Kodi simuli kunama m'dzanja langa lamanja?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa