Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Masalimo 139:24 - Buku Lopatulika

24 Ndipo mupenye ngati ndili nao mayendedwe oipa, nimunditsogolere panjira yosatha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Ndipo mupenye ngati ndili nao mayendedwe oipa, nimunditsogolere pa njira yosatha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Muwone ngati ndimatsata njira yoipa iliyonse, ndipo munditsogolere m'njira yanu yamuyaya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Onani ngati muli mayendedwe aliwonse oyipa mwa ine, ndipo munditsogolere mʼnjira yanu yamuyaya.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 139:24
17 Mawu Ofanana  

Odala angwiro m'mayendedwe ao, akuyenda m'chilamulo cha Yehova.


Ndidzathamangira njira ya malamulo anu, mutakulitsa mtima wanga.


Mundiphunzitse chokonda Inu; popeza Inu ndinu Mulungu wanga; Mzimu wanu ndi wokoma; munditsogolere kuchidikha.


Mundimvetse chifundo chanu mamawa; popeza ndikhulupirira Inu: Mundidziwitse njira ndiyendemo; popeza ndikweza moyo wanga kwa Inu.


Mudzandidziwitsa njira ya moyo, pankhope panu pali chimwemwe chokwanira; m'dzanja lanu lamanja muli zokondweretsa zomka muyaya.


Mwayesera mtima wanga; mwandizonda usiku; mwandisuntha, simupeza kanthu; mwatsimikiza mtima kuti m'kamwa mwanga simudzalakwa.


Mundiphunzitse njira yanu, Yehova, munditsogolere panjira yachidikha, chifukwa cha adani anga.


Yehova, munditsogolere m'chilungamo chanu, chifukwa cha akundizondawo; mulungamitse njira yanu pamaso panga.


Njira ya oipa inyansa Yehova; koma akonda wolondola chilungamo.


Wokhulupirira mtima wakewake ali wopusa; koma woyenda mwanzeru adzapulumuka.


Pakuti chipata chili chopapatiza, ndi ichepetsa njirayo yakumuka nayo kumoyo, ndimo akuchipeza chimenecho ali owerengeka.


Yesu ananena naye, Ine ndine njira, ndi choonadi, ndi moyo. Palibe munthu adza kwa Atate, koma mwa Ine.


Chifukwa chake monga momwe munalandira Khristu Yesu Ambuye, muyende mwa Iye,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa