Masalimo 139:2 - Buku Lopatulika2 Inu mudziwa kukhala kwanga ndi kuuka kwanga, muzindikira lingaliro langa muli kutali. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Inu mudziwa kukhala kwanga ndi kuuka kwanga, muzindikira lingaliro langa muli kutali. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Inu mumadziŵa pamene ndikhala pansi, pamenenso ndidzuka, mumazindikira maganizo anga muli kutali. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Inu mumadziwa pamene ndikhala pansi ndi pamene ndidzuka; mumazindikira maganizo anga muli kutali. Onani mutuwo |