Masalimo 138:3 - Buku Lopatulika3 Tsiku loitana ine, munandiyankha, munandilimbitsa ndi mphamvu m'moyo mwanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Tsiku loitana ine, munandiyankha, munandilimbitsa ndi mphamvu m'moyo mwanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Pa tsiku limene ndidakuitanani, Inu mudandiyankha, mumandilimbitsa mtima ndi mphamvu zanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pamene ndinayitana, munandiyankha; munandisandutsa wamphamvu ndi wolimba mtima. Onani mutuwo |